Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Mtukula Pakhomo Wapindulira Mabanja Ambiri ku Mulanje

Bungwe la OXFAM mdziko muno lati ndalama za ntchito ya mtukula pakhomo zapindulira anthu anthu ambiri m’boma la Mulanje. Mkulu wa bungweli mdziko muno a John Makina alankhula izi ndi Radio Maria pomwe...

View Article


Akhristu Awayamikira Kamba Kopulumutsa Montfort Press

Akhristu a mpingo wakatolika mu Arkdayosizi ya Blantyre awayamikira kamba ka mgwirizano omwe wathandiza kupulumutsa malo a mpingowu a Montfort Press. Arkepiskopi wa Arkdayosiziyi Ambuye Thomas Luke...

View Article


Papa Fransisko Wapempha Mayiko Athandize Kudzetsa Mtendere Mdziko La Syria

M’tsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse papa Fransisko wapempha mayiko kuti athandize kudzetsa mtendere m’dziko la Syria. Papa walankhula izi kamba kokhudzidwa ndi mavuto omwe anthu akupitilira...

View Article

Boma Lapempha Anthu Azibweretsa Mfundo Zothandiza

Anthu m’dziko muno awapempha akuti asamangokonda kulankhula mawu okhudza mbari zomwe dziko lino silinachite bwino koma kuti azibweranso ndi mfundo zomwe zingathandize pa chitukuko cha dziko lino. Nduna...

View Article

Ma Episkopi Adzipereka Pothetsa Mchitidwe Wozembetsa Anthu Mdziko la Phillipines

Ma Episkopia mpingo wakatolika m’dziko la Philllipines ati adzipereka pa ntchito yolimbana ndi m’chitidwe wozembetsa anthu umene wakula kwambiri m’dzikomo. Ma episikopi-wa wa alankhula izi pakutha pa...

View Article


Anthu Azisunga Agalu Osaposera Atutu Kuti Apewe Chiwewe

Matenda a chiwewe akuti angathe ngati anthu atamakhala ndi agalu osachepera atatu m’makomo mwawo. M’modzi mwa akuluakulu kuofesi yoona za nyama ya Vetenale ku Thondwe m’boma la Zomba a William...

View Article

Mafumu a Mizinda Mdziko la Rwanda Alamulidwa Kukakhala Kundende Moyo Wawo Wonse

Bwalo la milandu m’dziko la France lalamula mafumu awiri a mizinda ina ya m’dziko la Rwanda kuti akakhale kundende moyo wawo wonse kamba kokhudzidwa ndi mulandu wakuphedwa kwa anthu ochuluka m’chaka...

View Article

Dayosizi ya Chikwawa Ipempha Thandizo la Chakudya

Dayosizi ya mpingo wa katolika Chikwawayapempha anthu komanso mabungweakufuna kwabwino kuti athandize anthu okhala m’dera la kunsi kwa m’tsinje wa Shire omwe akhudzidwa kwambiri ndi mavuto a njala....

View Article


Kuwomberana kwa Mphamvu Kwabuka Mdziko la South Sudan

Kuwomberana kwa mphamvu kwabuka mu mzinda wa JUBA mdziko la South Sudan pakati pa asilikali aboma ndi asilikali a yemwe anali wachiwiri kwa mtsogoleri wa dzikolo. Kuwomberanaku komwe kunayamba...

View Article


Kalindo Watula Pansi Udindo Wake

Phungu wa ku nyumba ya malamulo m’dera la kum’mwera mwa boma la Mulanje a Elias Bon Kalindo wati kutula pansi kwa udindo wake kuthandiza pa ntchito zopititsa luso la zisudzo mdziko muno. A Kalindo...

View Article

Amayi Akatolika Athandiza Seminale ya Nankhunda

Amayi a mpingo wakatolika mu dayosizi ya Zomba ati amadziwa zakufunika kothandiza asemino omwe akuchita maphunziro awo pa seminale yaying’ono ya Nankhundamudayosizi-yi. Wapampando wa bungwe-li mu...

View Article

Kwaya One ya Mtsilo Yapindula ndi Radio Maria Malawi

Kwaya One ya Mtsilo ku parish ya Mponela mu arkidayosizi yaLilongwe ya mpingo wakatolika yati yapindula pa ulendo wake woyendera wailesi ya Maria ku Mangochi. Wapampando wa kwayayi a Rabson Joseph...

View Article

CCJP Yachita Misa Yopemphelera Anthu a Mtundu wa Chialubino

Bungwe la Chilungamo ndi mtendere mu Arkdayosizi ya Blantyre ya mpingo wakatolika lapitiriza kupempha anthu mdziko muno kuti adzipereke pothana ndi mchitidwe wozunza ndi kupha anthu a chialubino....

View Article


UN Yapempha Bata Mdziko la South Sudan

Nthambi yowona za chitetezo ku bungwe la United Nations (UN)lapempha magulu awiri omwe akumenyana mdziko la South Sudan kuti athetse kusamvana komwe kulipo pakati pawo pofuna kupewa zamtopola kuti...

View Article

Dayosizi ya Zomba Yapempha Ogwira Ntchito Mchipatala Akhale Olimba pa Chikhristu

Dayosizi ya Zomba ya mpingo wakatolika yapempha akhristu ogwira ntchito muzipatala kuti akhale olimba pa chikhristu chao komanso akuyenera kuzindikira kuti mpingo umawaganizira. Episkopi wa dayosiziyi...

View Article


Ana Opemphapempha Angachepe Ngati Makolo Ayika Chidwi pa Ana Awo

Chiwerengeo cha ana opemphapempha omwe amapezeka m’miseu ya m’mizinda ya dziko lino ati chingachepe ngati makolo atayika chidwi pa ana awo. Mkulu wa bungwe lowona za ana la Step Kids Awareness (STEKA)...

View Article

Anthu 8 Afa ndi Moto Mdziko la South Africa

Anthu asanu ndi atatu (8) afa ndi moto umene unabuka pa malo ena opelekerapo chisamaliro cha ana amasiye ndi ovutika a Key of Hopeku Durban m’dziko la South Africa. Malingana ndi malipoti a wailesi ya...

View Article


Ofesi ya Zamaphunziro Iyamikira Sukulu Ya St.Johns Nursery

Ofesi ya za maphunziro mu zoni ya Chimwala yayamikira sukulu ya m’mera mpoyamba ya St. John yomwe ili m’dera la a Senior Chief, Chimwala m’boma la Mangochikamba kodzipeleka pa ntchito zotukula...

View Article

Ntchito Yopereka Ziphaso Kwa Mzika Yayamba Mdziko Muno

Bungwe lolemba ndi kupereka ziphaso za m’dzika za dziko lino la National Registration Bureau (NRB) lati layamba ntchito yolemba komanso kupereka ziphaso-zi. M’neneri wa bungweli a Norman Fulatira ndi...

View Article

Amuna Awiri Amangidwa Kamba Koba Ndalama

Apolisi  m`boma la Mangochi akusunga muchitokosi amuna awiri  kaamba kowaganizira kuti  anathyola nyumba  ndi kuba ndalama. Malinga ndi  wachiwiri kwa ofalitsa nkhani za apolisi m’boma la Mangochi...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live