Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Canon Opuma wa Mpingo wa Anglican Atisiya

A ku likulu la chipani cha Anglican mu dayosizi ya Upper Shire mdziko muno akulengeza za imfa ya Canon Absalom Kasiya opuma omwe amwalira lero pa ngozi ya galimoto ku Liwonde. Maliro akulilira ku...

View Article


Sister Moyo Amwalira

A ku likulu la chipani cha Rosarian Sisters mu dayosizi ya Mzuzu alengeza za imfa ya Sister Maria Rita Moyo. Sister Moyo anabadwa mu chaka cha 1948 ndipo anachita malumbiro awo oyamba mu chipanichi pa...

View Article


Alamulidwa Kupereka 5 Sauzande Kamba Kopezeka Akugulitsa Malonda Malo Osayenera

Bwalo la milandu la Midima ku Limbe mu mzinda wa Blantyre lalamula anthu khumi ndi awiri 12 kuti apereke chindaputsa cha ndalama zokwana 5 sauzande aliyense kaamba kopezeka akuchita malonda pa malo...

View Article

Papa Ayikiza M’mapemphero Anthui Okhuzidwa ndi Chiwembu Mdziko la Turkey

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Fransisko anapempha mphindi yokhala chete pofuna kuyikiza mmapemphero anthu onse omwe akhudzidwa ndi chiwembu chomwe chachitika  pa bwalo lina la...

View Article

Radio Maria Malawi Yapempha Anthu Akwaniritse Malonjezo awo a Mariatona

Abwenzi a Radio Maria Malawi komanso anthu akufuna kwabwino awapempha kuti akwaniritse lonjezo lawo lothandiza wailesiyi pamene Mariatona wa chaka chino akupita kumapeto. Wapampando wa Mariatona ya...

View Article


Dziko la Turkey Lakhazikitsa Lachinayi Ngati Tsiku Lapadera

Dziko la Turkey lakhazikitsa tsiku la lachinayi pa 30 June, 2016 kukhala lapadera mdzikolo pofuna kukhudza maliro a anthu 42 omwe afa pa chiwembu chomwe chachitikira  pa bwalo la ndege mu mzinda wa...

View Article

Mphunzitsi Amangidwa Kamba Kogwilirira Mwana wa Sukulu

Apolisi m’boma la Ntchisi amanga mphunzitsi wa pa sukulu ina ya pulayimale kamba kogwirira ophunzira wina pa sukulupo wa zaka 16 zakubadwa. Mneneri wa apolisi m’bomalo Sergent  Gladson M’bumpha...

View Article

Zokonzekera Kutsekera Radio Maria Malawi Mariatona Zili Mchimake

Pali chiyembekezo chakuti mwambo wotsekera Radio Maria Mariatona ku phiri la Michiru ku Arkdayosizi ya Blantyre ya mpingo wakatolika loweruka ukhala wopambamba kamba koti zonse zokonzera tsikuli ati...

View Article


Msonkhano Waukulu Wachiri Wa ECM Watha

Msonkhano waukulu wachiwiri wa pachaka wa ma episkopi a mpingo wakatolika mdziko muno watha lero ku likulu la mpingowu mu mzinda wa Lilongwe. Polankhula ndi Radio Maria Malawi pambuyo pa msonkhanowu...

View Article


Woyimira Anthu pa Milandu Wapezeka Atafa Mdziko la Kenya

Loya wina yemwe amayimilira  munthu wina pamlandu woti apolisi m`dziko la Kenyaakumachitira nkhanza  anthu m`dzikolo wapezeka  atafa munzinda wa Nairobi m`dzikolo. Loyayu, Willie Kimani wa zaka 32,...

View Article

Ma Episkopi Mdziko la South Africa Adzudzula Ziwawa Mdzikolo

Maepiskopi a mpingo wakatolika mdziko la South Africa adzudzula  mchitidwe wa ziwawa omwe ukuchitika mdzikolo potsatira chisankho cha makhansala chomwe chikuyembekezeka kuchitika mwezi wa mawa. Malinga...

View Article

Chitukuko Chingapite Patsogolo Ngati Adindo ndi Mzika Akulumikizana

Kulumikizana pa nkhani za chitukuko cha m’madera pakati pa adindo komanso mzika ati ndi njira yokhayo yomwe ingapititse patsogolo chitukuko cha dziko lino. Wachiwiri kwa mfumu ya mzinda wa Blantyre, a...

View Article

Katsonga Wapempha Akhristu Azithandiza Radio Maria Malawi

Akhristu a mpingo wakatolika m`dziko muno awapempha adzitenga  gawo lalikulu pothandiza Radio Maria Malawi. Yemwe anali mlendo wolemekezeka pa mwambo wotsekera ntchito yotolera thandizo la wailesiyi...

View Article


Amuna Awiri Amangidwa Kamba Kobera Mayeso a MSCE

Amuna awiri ali m’manja mwa apolisi atapezeka akubera mayeso a fomu 4 m’boma la Balaka. M’modzi mwa amunawa a Joseph Makiyi omwe amagwira ntchito ku Prison Fellowship anatenga tchuthi kuntchito kwawo...

View Article

Alamulidwa Kukakhala ku Ndende Zaka 10 Kamba Kopereka Mimba kwa Mtsikana...

Mwamuna wina wa zaka 18 zakubadwa amulamula kuti akakhale kundende ndikukagwira ntchito ya kalavula gaga kwa zaka khumi (10) kamba kopereka mimba kwa msungwana wa zaka 15 m’boma la Mwanza. Mneneri wa...

View Article


Papa Wapepesa Anthu Amene Akhuzidwa Ndi Chiwembu Mdziko la Bangladesh

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Fransisko wapereka uthenga wa chipepeso kwa anthu omwe akhudzidwa ndi chiwembu chomwe chaphetsa anthu makumi awiri mu mzinda wa Dhaka mdziko la...

View Article

Mutharika Wati Atukula Mzinda wa Zomba

President wa dziko lino Professor Arthur Peter Mutharika wati boma lake likhazikitsa zitukuko zosiyanasiyana mu mzinda wa Zomba ndi cholinga choti mzindawu udzifanafana ndi mizinda ina ya mdziko...

View Article


Papa Francisco wati Ntchito za Migodi Zikomere Anthu Okhala Moyandikana ndi...

Mtsogoleri wampingo wakatolika padziko lonse Papa Francisco,wapempha mayiko kuti adziwonetsetsa kuti ntchito za migodi zomwe zikuchitika mmayiko awo zikuchitika mokomera anthu  onse maka oyandikana ndi...

View Article

Atsogoleri a Zipani Zotsutsa Sapikisana Nawo pa Chisankho cha Pulezidenti...

Pamene chisankho cha pulezidenti mdziko la Burundi chikuyembekezeka kuchitika lachiwiri, mtsogoleri wa dzikolo Pierre Nkurunziza ati akuyembekezeka kupambana pa chisankhochi zomwe zichititse kuti...

View Article

Ambuye Musikuwa Apempha Asisiteri Akhale Odzipereka pa Utumiki

Episkopi wa dayosizi ya Chikwawa ya mpingo wakatolika Ambuye Peter Musikuwa wapempha asisteri kuti azikhala odzipereka pa utumiki wao. Ambuye Musikuwa alankhula izi pa mwambo wa malumbiro a ku nthawi...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>