Papa Wapepesa Dziko la Mexico, America
Mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko lonse Papa Fransisko wapereka uthenga wachipepeso kwa anthu omwe akhuzidwa ndi mphepo ya mphamvu yomwe yakhuza anthu a m’maiko a Mexico komanso America....
View ArticleAfa Atatsamwidwa ndi Chingamu
M`nyamata wina wa zaka zisanu ndi ziwiri (7) wafa atatsamwidwa ndi chingamu ku Bangwe munzinda wa Blantyre. Malinga ndiwothandizira mu ofesi yazofalitsa nkhani pa polisi ya Limbe, Sergent Widson...
View ArticleBambo Albert Chandiyang`ana Alowa M’manda
Mwambo woika m`manda thupi la Bambo Albert Chandiyang`ana amu arkidayosizi ya Blantyrewachitika lachinayi ku ku St. Louis Montfort CI Parish mu arkidayosiziyo. Mwambowu unayamba ndi msembe ya...
View ArticleAnthu 7 Afa Pa Ngozi Ku Ntcheu
Anthu asanu ndi awiri 7 afa ndipo ena avulala basi yomwe anakwera itagwa pa Mlangeni m`boma la Ntcheu. Wofalitsa nkhani za apolisi m`bomali a Gift Matewere atsimikiza zankhaniyi ndipo ati basiyi...
View ArticleCOOPI Ikulimbikitsa Kudzidalira Kwa Anthu Amene Akhudzidwa Ndi Ngozi Zogwa...
Bungwe la Cooperazione Internazionale (COOPI) lati liwonetsetsa kuti likupititsa patsogolo kudzidalira kwa anthu amene akhudzidwa ndi ngozi zogwa mwadzidzidzi mdziko muno. Wamkulu wa bungweli mdziko...
View ArticleOfalitsa Nkhani Aboma Awalangiza Kuphunzitsa Anthu Zandondomeko za Ntchito za...
Anthu ogwira ntchito m`maofesi ofalitsa nkhani aboma ochokera m`maboma osiyanasiyana awalangiza kuti akhale patsogolo kuphunzitsa anthu zandondomeko za ntchito za boma. Nduna yazofalitsa nkhani...
View ArticleMpingo Wakatolika Upitiriza Kufalitsa Uthenga, Kuthandiza Boma Kudzera Mu...
Mpingo wa katolika m’dziko muno wati kudzera mu chipani cha mofolo woyera upitiriza kufalitsa uthenga wa Mulungu ponseponse ndi cholinga chokuti akhristu ake azame mu chikhristu chawo. Episkopi wa...
View ArticleDziko la Nigeria Lalengeza Kuti Lichita Kampeni Yopereka Katemera Wa Matenda...
Dziko laNigeria lalengeza kuti lichita kampeni yopereka katemera wothana ndi matenda a Polio, potsatira kubukanso kwa matendawa m`dzikolo. Malinga ndi malipoti awailesi ya BBC, ana awiri alumala...
View ArticlePapa Ayendera Amayi 20 Omwe Anazembetsedwa M’maiko Awo
Mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko lonsePapa Francisco wayendera amayi makumi awiri (20) omwe anabedwa ndi kuzembetsedwa kuchokera ku maiko awo ndikukagulitsidwa ku maiko ena cholinga choti...
View ArticleBoko Haram Yatulutsa Kanema Yowonetsa Atsikana Omwe Ikusunga
Gulu la za uchifwamba mdziko la Nigeria la Boko Haram latulutsa kanema yowonetsa ena mwa atsikana omwe gululi linagwira mdera la Chibok ndipo likuwasunga. Malinga ndi malipoti a wasilesi ya BBC,...
View ArticleBungwe la SCORE_ECD Lati Lipitiriza Kusula Alezi a Sukulu za Mkombaphala
Bungwe la Strengthen Capacity of Religious Women In Early Childhood Development (SCORE-ECD) lati lipitiriza kusula alezi a msukulu za mkombaphala za chikatolika mdziko muno ndi cholinga chopititsa...
View ArticleBoma Liyamba Kugawa Chakudya Posachedwapa
Boma lati liyamba kugawa chakudya posasedwapa m’maboma onse omwe akhudzidwa ndi vuto la njala m’dziko muno. Nduna ya zofalitsa nkhani ndi kuphunzitsa anthu wolemekezeka mayi Patricia Kaliati anena izi...
View ArticleAmalawi Agwirane Manja Potukula Ntchito Zaumoyo
Anthu m`dziko muno awapempha kuti agwirane manja ndi boma polimbikitsa ntchito za umoyo. Mkulu wa bungwe lothandiza anthu osowa la Chisomo Support for The Needy a Mcsayitings Mdoka alankhula izi mu...
View ArticleAnthu 30 afa Pachiwembu Mdziko la DRC
Anthu makumi atatu (30),afa gulu la zauchifwamba litachitira chiwembu mudzi wina m`dziko la Democratic Replican of Congo (DRC). Guluri ati linachitira chiwembu mudzi Rwagomaomwe uli pafupi ndi tawuni...
View ArticleCanon Chizito a Mpingo wa Anglican Amwalira
Dayosizi ya Upper Shire ya mpingo wa Anglican yalengeza za imfa ya wansembe wopuma wa mpingowu Canon Arthur Chizito. Malinga ndi chikalata chomwe akulikulu la dayosiziyi atulutsa Canon Chizito amwalira...
View ArticlePatel Apempha Mabungwe Ayambiretu Kulimbikitsa 50-50 Campaign
Boma komanso mabungwe omwe amalimbikitsa kuti pasakhale kusiyana pakati pa amuna komanso akazi awapempha kuti ayambe pano kulimbikitsa kampeni yomema anthu kuti avotere amayi ku nyumba ya malamulo ya...
View ArticleArkibishop Msusa Apempha Akhristu Akhale Ogwirizana Monga Apostoli
Akhristu a mpingo wa katolika awapempha kuti akhale ogwirizana monga m`mene apostoli oyamba aja ankachitira atalandira mphamvu za mzimu oyera. Arkepiscopi wa archdayosizi ya Blantyre wolemekezeka...
View ArticlePapa ndi Okhudzidwa ndi Imfa ya Anthu Anayi Mdziko la Portugal
M’tsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse papa Francisco wati ndi wokhudzidwa ndi imfa ya anthu anayi omwe afa kamba ka ngozi ya moto wachilengedwe umene unabuka mu nkhalango ina m’dziko la...
View ArticleCADECOM Yapempa Atolankhani Kuti Alimbike Pothana Ndi Matenda A Kunyentchera
Nthambi yoona za chitukuko mu mpingo wa katolika ya Catholic Development Committee (CADECOM) mu dayosizi ya Zomba yati atolankhani ali ndi udindo waukulu ophunzitsa anthu kuyipa kwa matenda...
View ArticleAphunzitsi Achikatolika M’boma La Zomba Awayamikira Kamba Kothandiza Odwala
Aphunzitsi abungwe la chikatolika ku parish ya Mayaka m’boma la Zomba awayamikira chifukwa cha chidwi chawo chofuna kuthandiza odwala. Mmodzi mwa akulu akulu pa chipatala cha chikulu cha Zomba Mayi...
View Article