Quantcast
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Papa Alandira a Kazembe a Mmayiko Ena

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco analandira akazembe a mmaiko a Estonia, Malawi, Namibia, Seychelles, Thailand ndi Zambia komwe akazembewa amapereka makalata awo...

View Article


Mwambo Wodzoza Udikoni

Mwambo wodzoza asemino 13 kukhala adikoni wachitika Loweruka pa 21 May 2016 Ku Zomba Cathedral mu dayosizi ya Zomba ndipo Ambuye Desmond Tambala episkopi wa Dayosiziyi ndi amene azodza adikoniwa ....

View Article


Akhristu Eni Azipereke Polimbikitsa Mpingo Wozidalira

Atsogoleri atsopano a bungwe loyimira akhristu eni mu mpingo wakatolika awapempha kuti adzipeleke pa ntchito yolimbikitsa akhristu pa za mpingo wodzidalira. Mlangizi wa bungwe-li mu mpingo wa katolika...

View Article

Katswiri Wazisuzo ‘Izeki’ Wamwalira

Mmodzi mwa akatswiri azisuzo mdziko muno John Nyanga yemwe amatchuka ndi dzina loti Izeki wamwalira lamulungu masana ku chipatala chachikulu cha Queen Elizabeth mu mzinda wa Blantyre. Mzake yemwe...

View Article

Mabungwe A Mipingo Athandize Pa Bilu Ya Migodi

Bungwe la Norwegian Church Aid m’dziko muno lapempha mabungwe omwe si a boma makamaka amene ali amipingo kuti athandize boma pa ndondomeko yowunikiranso bwino bilu ya migodi. Mkulu wa bungwe la...

View Article


Apempha Akhristu Athandize Seminale Ya St. Peters

Akhristu a mpingo wakatolika m’dziko muno awapempha akuti adzipeleke pa ntchito yosamalira seminale yayikulu ya St. Peters yomwe ili mu Dayosizi ya Zomba. Mkulu woyendetsa ntchito za seminalyi bambo...

View Article

MOAM Yakhumudwa Ndi Anthu Okwera Minibus

Bungwe la eni minibus m’dziko muno laMinibus Owners Association of Malawi (MOAM) lati ndilokhumudwa  kuti anthu okwera ndi amene akuthandizira kuti ma minibus  m’dziko muno azinyamula anthu mopyola...

View Article

Mpingo Udzudzula Boma Polanda Malo Kwa Anthu Akumidzi

Mpingo wa katolika m`dziko la Angolawa dzudzula m`chitidwe wa akuluakulu a boma omwe akumalanda malo anthu a kumidzi ndi ku ma kawapeleka kwa anthu a bizinesi . Malinga ndi wailesi ya Vatican, Episkopi...

View Article


Parish Ya St. Anna Ichita M’bindikiro

Parish ya mpingo wakatolika ya  St. Anna ku Kapire    mu dayosizi  ya Mangochi yati imadziwa zakufunika kolimbikitsa moyo wauzimu pakati pa akhristu ake. Bambo mfumu a parishi-yi bambo Danasio Malajira...

View Article


UTATU WOYERA NDI CHIPHUNZITSO CHA UMODZI

Amayi a  mpingo wa katolika omwe amatumikira Mulungu kudzera m`maimbidwe  awapempha kuti azikhala ogwirizana monga Utatu oyera wa Mulungu atate,Mulungu mwana ndi Mulungu mzimu oyera. Sister Agatha...

View Article

ANTHU OTHAWA KWAO ASIMBA LOKOMA

Dziko la Greece  layamba kusamutsa anthu ena othawa kwawo omwe amakhala  pa malo ena otchedwa idomeni ndikukawaika ku malo ena kufupi ndi malire a dziko la Macedonia. Malingana ndi malipoti a wailesi...

View Article

Anthu Atatu Afa pa Chiwonetsero cha Zipani Zotsutsa Mdziko la Kenya

Anthu atatu afa kumvuma kwa dziko la Kenya potsatira ziwonetsero zosakondwa za zipani zotsutsa boma zofuna kuti bungwe loyendetsa chisankho mdzikolo lisinthe ena mwa malamulo ake. Malipoti a wailesi ya...

View Article

Anthu Khumi Afa pa Ngozi ya Bus

Anthu khumi afa ndipo ena 62 avulala bus yomwe anakwera itachita ngozi mdera la Songo mdziko la Mozambique. Malinga ndi malipoti bus-yo yomwe ndi ya Kampani ya Nyamende nambala yake KMZ 56 ZN...

View Article


Bungwe la CFT Lakonza Ndondomeko Zokweza Malonda Mdziko Muno

Bungwe lowonetsetsa kuti pakukhala chilungamo pa nkhani za malonda komanso kuteteza anthu ogula m’dziko muno, la Competition and Fair Trading (CFT) lati lakonza ndondomeko za tsopano zomwe zithandize...

View Article

Papa Wati Kuyera Sikuchita Kugulidwa

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha akhristu kuti ngati akufuna kudzakhala oyera, sakuyenera kuchita manyazi potsatira zomwe Mulungu amafuna. Papa amalankhula izi pa...

View Article


Akhristu Akatolika Akonzekere Bwino Lamulungu La Pa 29 May 2016

Mpingo wakatolika m’dziko muno wapempha akhristu a mpingowu kuti akonzekere bwino tsiku la mulungu la pa 29May2016pomwe akhristu a mpingowu apemphedwa kuti adzathandize seminale ya StPeter’s yomwe ili...

View Article

Papa Wati Ndi Udindo Wa Aliyense Kusamalira Ndi Kuteteza Ana

M'tsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse PapaFrancisko wati ndi udindo wa munthu aliyense kuwonenetsetsa kuti ana akulandira chisamaliro ndi chitetezo chabwino. Papa walankhula izi lachitatu...

View Article


Asilikali Apulumutsa Ana 53 Omwe Anabedwa Ku Ethiopia

Asilikali m’dziko la Ethiopia ati akwananitsa kupulumutsa ana makumi asanu ndi atatu 53 omwe anabedwa ndi gulu lina la zigawenga m’dzikomo. Malingana ndi malipoti a wailesi ya BBC anawa akuti anagwidwa...

View Article

Ulendo wa Ku Uganda Wapsya

Bungwe la abwenzi a amalitiri aku Uganda lati zokonzekera za ulendo wokayendera malo oyera a Namugongo  omwe amalitiri anaphedwera m’dziko la Uganda chaka chino zayenda bwino. Malinga ndi wapampando wa...

View Article

Bungwe la CCJP Lipempha Boma Lilipire Msanga Aphunzitsi ku Nsanje

Bungwe la chilungamo ndi mtendere mu dayosizi ya Chikwawa ya mpingo wakatolika yapempha boma kuti likonze msanga malipiro a aphunzitsi a m’boma la Nsanje omwe mpaka pano sanalandire malipiro awo a...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>