Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Boma la Iraq Lalanda Nyumba Momwe Mumakhala Zigawenga za Islamic State

Boma la dziko la Iraq lalanda nyumba yake yomwe mumapezeka zigawenga za chisilamu za Islamic State mu mzinda wa Fallujah mdzikolo. Malinga ndi malipoti a wailesi ya BBC akuluakulu a gulu la zigawengazi...

View Article


Chipatala cha Dedza Chapempha Mafumu Kuti Alimbikitse Uchembere Wabwino

Chipatala cha boma cha Dedza chapempha mafumu kuti apitilize kulimbikitsa amayi oyembekezera kuti azichilira ku chipatala. Ofalitsa nkhani za chipatalachi, a Alnod Ndalira, wanena izi potsekulira...

View Article


Bungwe la YODEP Likukhazikitsa Mabungwe Othana ndi Nkhanza kwa Ana ndi Amayi

Bungwe la Youth Development and Productivity (YODEP)m’boma la Zomba  lati ntchito yokhazikitsa ma bungwe a abambo omwe akhale akuteteza amayi ndi ana ku nkhanza zosiyanasiyana ikuyenda bwino. Mmodzi...

View Article

Ambuye Msusa Ayamikira Akhristu a Parishi ya Bvumbwe

Akhristu a mpingo wakatolika mu arkidayosizi ya Blantyre awayamikira kamba kochilimika pa zampingo wodzidalira pomwe akugwira ntchito za chitukuko m`maparishi awo.   Arkiepiskopi wa dayosiziyi, Ambuye...

View Article

Ambuye Stima Ayamikira Ophunzira Akale a Sukulu ya St. Paul The Apostle

Anthu omwe anaphunzira pa seminale yaying’ono ya St. Paul the Apostle, mu dayosizi ya Mangochi ya mpingo wakatolika, awayamikira kamba kotengapo gawo popititsa patsogolo chitukuko cha dayosiziyi....

View Article


Bungwe la FAWO Lati Amayi Amasiye Akhale Odzidalira

Bungwe lomenyela ufulu wa amayi ndi ana amasiye mdziko muno la Foundation for Widows and Orphans (FAWO) lati nthawi yakwana yoti amayi amasiye akhale odziyimira pawokha pa nkhani za chuma. Polankhula...

View Article

Papa Wati Chilango cha Kupha ndi Chosayenera

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Fransisko wati chilango chakupha ndi chosayenera kamba koti munthu aliyense ali ndi ufulu wokhala ndi moyo. Papa amalankhula izi potsatira msonkhano...

View Article

Nyumba Zosindikiza Ndi Kuwulutsa Nkhani Zizilemba Mwaukadaulo Nkhani Zokhudza...

Nyumba zotsindikiza ndi kuwulutsa nkhani mdziko muno azilimbikitsa kuti zizifufuza mokwanira komanso kulemba mwaukadaulo nkhani zokhudza anthu olumala. Wachiwiri kwa mkulu wa nthambi yophunzitsa...

View Article


PRO-LIFE Yati Kupha ma Alubino ndi Kutsutsana ndi Cholinga cha Mulungu

Bungwe loteteza miyoyo ya anthu la mpingo wa katolika la PRO-LIFE lati kupha anthu a mtundu wa chialubino ndi kutsutsana ndi cholinga cha Mulungu kaamba koti iye analenga munthu aliyense m’chifaniziro...

View Article


Mpingo Wakatolika Wati Pasakhale Lamulo Lakupha Munthu Wopha ma Alubino

Mpingo wa katolika mdziko muno wati ukugwirizana ndi ganizo la boma loti pasakhale lamulo lakupha  munthu wopezeka olakwa pa mlandu wosowetsa komanso kupha anthu a mtundu wa chialubino. Mlembi wa mkulu...

View Article

YCW Ikutolera Thandizo la Seminale Ya St. Peters

Bungwe la achinyamata mu mpingo wakatolika m’dziko muno la Young Christian Workers (YCW) lati likutolera thandizo pofuna kuthandiza seminale yaikulu ya St. Peters mu dayosizi ya Zomba yomwe padakali...

View Article

CCJP Yadzudzula Aphungu Ena Kamba Kosamapita Kunyumba Ya Malamulo

Bungwe la mpingo wakatolika la chilungamo ndi mtendere la Catholic Commission for Justice and Peace (CCJP) ladzudzula aphungu a ku nyumba ya malamulo kamba ka chisankho chomwe ena mwa iwo akuchita...

View Article

Boma Latsimikiza Kuti Zitukuko Zitha Posachedwa M’boma La Machinga

Anthu a m’madera a mafumu a Chiwalo komanso Kapoloma m’boma la Machinga awatsimikizira kuti zitukuko zomwe zikugwiridwa m’madera awo zifika kumapeto posachedwapa. Nthandizi wa nduna ya za nyumba ndi...

View Article


TEVETA Yati Ntchito Zake Zotolera Msonkho Ziyamba Kuyenda Bwino

Bungwe la Technical Interprenual Vocational Education and Training Authority (TIVETA) lati ntchito yake yotolera misonkho iyamba kuyenda bwino kaamba ka mgwirizano omwe bungweli wasayinirana ndi bungwe...

View Article

Atumiki a Radio Maria Malawi Awapempha Akhale Olimbikira Pofalitsa Uthenga wa...

Anthu omwe amagwira ntchito modzipereka ku Radio Maria Malawi awalimbikitsa kuti asamabwelere m’mbuyo pomwe akukumana ndi zovuta pa nthawi yomwe akutumikira. Bambo Edwin Lambulira alankhula izi...

View Article


Msonkhano wa PMS Watha Lachisanu

M’sonkhano waukulu wa masiku anayi wa atsogoleri oyendetsa ma bungwe a utumiki wa a Papa m’ma dayosizi onse ampingo wakatolika mdziko muno watha lachisanu. Polankhula pambuyo pa msonkhanowu omwe...

View Article

Papa Walimbikitsa Ubale wa Mpingo wa Katolika ndi Orthodox

Mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko lonse Papa Fransisko wapempha kuti mgwirizano omwe ulipo pakati pa mpingowu ndi mpingo wa Orthodox upitilire kuyenda bwino. Papa amalankhula izi la mulungu...

View Article


Mpingo Wa Anglican Wadzodza Ansembe Atatu

Mpingo wa Anglican mu dayosizi ya Upper Shire loweruka wadzoza madikoni atatu kukhala ansembe. Polankhula pa mwambowu Episkopi wa dayosiziyi Ambuye Brighton Vita Malasa ayamikira ansembe atsopanowa...

View Article

Zigawenga za Boko Haram Zapha Anthu Pafupifupi 150 Sabata Ino

Zigawenga za Boko Haram zapha anthu pafupifupi zana limodzi ndi makumi asanu sabata ino mchigawo cha Borno mdziko la Nigeria. Anthu omwe awona izi zikuchitika awuza wailesi ya BBC kuti anthu a mfuti...

View Article

Mpingo wa Anglican Ukuphunzitsa Anthu za Kuyipa Kozembetsa ndi Kupha ma Alubino

Mpingo wa Anglican mdziko muno wati wayamba ntchito yophunzizitsa ndi kudziwitsa anthu za kuyipa kwa mchitidwe wopha ndi kuzembetsa anthu a mtundu wa chi alubino womwe padakali pano wakula mdziko muno....

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>