Quantcast
Channel: Radio Maria Malawi
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live

Anthu 5 Afa Kaamba ka Moto Mdziko la California

Anthu asanu ndi anayi afa ndipo pali chiyembekezo chakuti chiwerengero cha anthuwa chikhoza kukwera potsatira moto wamphamvu omwe unabuka mnyumba ina  mdera la Oakland mu mzinda wa California. Malinga...

View Article


Sisteri Aphedwa Mdziko la Congo

Sisteri wina wa chipani cha Franciscan mdziko la Congo ati waphedwa mdera la Bakavu pa sukulu yomwe amagwirapo ntchito. Malinga ndi malipoti a wailesi ya Vatican anthu awiri omwe anatenga mipeni...

View Article


Akhristu Afunitsa Kutsata Moyo wa Francis Chaviyere Woyera

Akhristu a pa tchalichi laFrancis Chaviyere  Woyeraku NamweramuDayosiziya Mangochiati apitiriza kudzipereka pa ntchito yofalitsa uthenga wabwino monga momwe nkhoswe yawo inali kuchitira. Wapampando wa...

View Article

Anthu 5 Afa pa Ngozi pa Msika wa Rudoviko M’boma la Ntcheu

Anthu asanu 5 afa ndipo ena ambiri avulala pa ngozi ya pa nsewu yomwe yachitika pa msika wa Rudoviko m’boma la Ntcheu. Wofalitsa nkhani za apolisi m’bomali Sergeant Gift Matewere watsimikiza za...

View Article

Njala Ikuyembekezeka Kuchepa M’boma la Chikwawa

Vuto la njala akuti likuyembekezeka kuchepa m’boma la Chikwawa potsatira ndondomeko yabwino ya ulimi wa nthilira imene yakhadzikitsidwa m’bomalo. Mkulu wowona za ndondomeko za chitukuko m’bomalo a...

View Article


Papa Wapempha Atsogoleri Alimbikitse Ulamuliro Wabwino

M’tsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse PAPA FRANCISCO wapempha atsogoleri a amayiko pa dziko lonse kuti alimbikitse ulamuliro wabwino pakati pa anthu omwe akuwatsogolera. Papa walankhula izi...

View Article

Kusamalira Anthu ndi Kusamalira Chilengedwe-Papa

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wauza akuluakulu a mpingowu owona za utumiki kuti kusamalira anthu ndi njira imodzi yosamaliranso chilengedwe. Malinga ndi uthenga omwe...

View Article

Amangidwa Kamba Kogwililira Msungwana wa Zaka 12

Apolisi m’boma la Dowa akusunga m’chitokosi bambo wina wa zaka 34 zakubadwa kwamba komuganizira kuti wagwilira mwana wa zaka 12m’bomalo. Malingana ndi ofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo Sergeant...

View Article


Ophunzira Achita Zionetsero Posakondwa ndi Kudula Mitengo

Ophunzira a sukulu ya pulaimale ya Nthumbi m’boma la Ntcheu anayenda ulendo wa ndawala posonyeza kusakondwa ndi kudula mitengo mwa chisawawa komwe kukuchitika m’madera ozungulira sukuluyo. Polankhula...

View Article


Kubwera Kwa Yesu Kudzetse Mtendere - Papa

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika padziko lonse Papa Fransiscowapitiriza kupempha akhristu kuti kubadwa kwa Yesu Khristu kudzabweretse Chilungamo, mtendere komanso chimwemwe mmitima mwawo. Papa...

View Article

Brother Henry Ibrahim a Chipani cha FIC Amwalira

Akulikulu la chipani cha ablazala mu mpingo wakatolika cha Brothers of Immaculate Conception of the Blessed Virgin Mary (FIC) ku Mzedi mu Arkdayosizi ya Blantyre alengeza za imfa ya Brother Henry...

View Article

Aphunzitsi Akukolezera Kuti Ana Aakazi Azisiyira Sukulu Panjira

Ophunziraa msukulu za pulaimale m’boma la Salima adandaula kaamba ka makhalidwe a aphunzitsi ena omwe ati akukolezera kuti ana aakazi azisiyira sukulu panjira. Ophunzirawa anena izi pa sukulu ya...

View Article

Papa Apempha Akazembe Kuti Adzetse Mtendere

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse Papa Francisco wapempha akazembe a m’maiko kuti awonenetsetse kuti akudzetsa mtendere popewa za mtopola mu ulamuliro wao. Malinga ndi malipoti a wailesi...

View Article


Papa Alimbikitsa Kufunika kwa Akhristu

Mtsogoleri wa mpingo wakatolika pa dziko lonse PapaFrancisco wauza ansembe kuti akuyenera kutumikira anthu nthawi zonse osati kuti azikhala patsogolo kupanga mfundo zoyendetsera mpingo kaamba koti...

View Article

Milandu ya Katengale ya Pulezidenti Zuma Iwunikidwenso

Bwalo lamilandu mdziko la South Africa lati ganizo lothetsa milandu 7 hundred 83 ya katangale ya pulezidenti wa dzikolo Jacob Zuma likuyenera kuwunikidwanso. Malipoti a wailesi ya BBC ati milanduyi...

View Article


Mutharika Wasintha Maudindo Ena

Mtsogoleri wa dziko lino Professor Arthur Peter Mutharika wasintha ena mwa ma udindo a m’boma potsatira mphamvu zomwe ali nazo kuchokera mmalamulo oyendetsera dziko lino. Malinga ndi chikalata chomwe...

View Article

Atolankhani 57 Aphedwa Chaka Chino

Atolankhani 57 ati ndi omwe aphedwa chaka chino pa nthawi yomwe amagwira ntchito yawo. Malinga ndi malipoti a News 24 atolankhaniwa 19 anaphedwa mdziko la Syria, khumi mdziko la Afghanstan, 9 mdziko la...

View Article


Afa Atawombedwa ndi Chiphaliwali

Mamuna ndi mkazi wake ati afa chiphaliwali chitawaomba mmudzi mwa Chilinda kwa mfumu yaikulu Makanjira m’boma la Mangochi. Wachiwiri kwa ofalitsa nkhani za apolisi m’bomali Sergent Amina Daudi wauza...

View Article

Anthu M’boma la Mangochi Akuvutikira Fetereza wa Makoponi

Anthu okhala m’boma la Mangochi ati akukumana ndi mavuto kuti agule fetereza otsika mtengo wa makoponi chaka chino. Izi zadziwika pamene Mtolankhani wathu anafika ku malo ogulitsira feterezayu komwe...

View Article

Ana Awiri Akokoloka ndi Madzi a Mvula

Ana awiri akokoloka ndi madzi a mvula mu mtsinje wa Thang’ande m’boma la Neno. Wofalitsa nkhani za apolisi m’bomalo Sergeant Raphael Kaliati wati anawa ndi Aufi Chiwembukomanso Benina Matemba onse a...

View Article
Browsing all 1875 articles
Browse latest View live


<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>